LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • CO-pgm20 masa. 4-5
  • Tsiku Laciŵili

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tsiku Laciŵili
  • Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2020
  • Nkhani Zofanana
  • Tsiku Laciŵili
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2021
  • Tsiku Lacitatu
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2020
  • Tsiku Laciŵili
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2019
  • Tsiku Loyamba
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2024
Onaninso Zina
Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2020
CO-pgm20 masa. 4-5
Zithunzi: 1. Mboni za Yehova zili mu ulaliki ndipo ni zokondwela. Mmodzi wa iwo ni wolemala ndipo akuyendetsedwa pa njinga ya olemala. 2. Wa Mboni za Yehova akambilana mfundo za m’Baibo na munthu wa mtundu wa Amishi. 3. Nehemiya.

TSIKU LACIŴILI

“Nyadilani dzina lake loyela. Mtima wa anthu ofunafuna Yehova usangalale”​—Salimo 105:3

KUM’MAŴA

  • 8:20 Vidiyo ya Nyimbo

  • 8:30 Nyimbo Na. 53 na Pemphelo

  • 8:40 YOSIILANA: Pezani Cimwemwe pa Nchito Yopanga Ophunzila​—Nolani Maluso Anu

    • • Kufunsa Mafunso (Yakobo 1:19)

    • • Lolani Mphamvu ya Mawu a Mulungu Kugwila Nchito (Aheberi 4:12)

    • • Kuseŵenzetsa Mafanizo Pofotokoza Mfundo Zofunika Kwambili (Mateyu 13:34, 35)

    • • Kukamba Mwaumoyo Pophunzitsa (Aroma 12:11)

    • • Kuonetsa Cifundo (1 Atesalonika 2:7, 8)

    • • Kuŵafika pa Mtima Anthu (Miyambo 3:1)

  • 9:50 Nyimbo Na. 58 na Zilengezo

  • 10:00 YOSIILANA: Pezani Cimwemwe pa Nchito Yopanga Ophunzila​—Landilani Thandizo la Yehova

    • • Zida Zofufuzila (1 Akorinto 3:9; 2 Timoteyo 3:16, 17)

    • • Abale Athu (Aroma 16:3, 4; 1 Petulo 5:9)

    • • Pemphelo (Salimo 127:1)

  • 10:45 UBATIZO: Mmene Ubatizo Wanu Ungakubweletseleni Cimwemwe Cacikulu (Miyambo 11:24; Chivumbulutso 4:11)

  • 11:15 Nyimbo Na. 79 na Kupumula

KUMASANA

  • 12:35 Vidiyo ya Nyimbo

  • 12:45 Nyimbo Na. 76

  • 12:50 Mmene Abale Athu Akupezela Cimwemwe pa Nchito Yopanga Ophunzila . . .

    • • mu Africa

    • • ku Asia

    • • ku Europe

    • • ku North America

    • • ku Oceania

    • • ku South America

  • 13:35 YOSIILANA: Thandizani Maphunzilo Anu a Baibo . . .

    • • Kudzidyetsa Okha Kuuzimu (Mateyu 5:3; Yohane 13:17)

    • • Kumapezeka pa Misonkhano (Salimo 65:4)

    • • Kupewa Mayanjano Oipa (Miyambo 13:20)

    • • Kuleka Makhalidwe Odetsa (Aefeso 4:22-24)

    • • Kukhala pa Ubale Wolimba na Yehova (1 Yohane 4:8, 19)

  • 14:30 Nyimbo Na. 110 na Zilengezo

  • 14:40 SEŴELO LA M’BAIBO: Nehemiya: “Cimwemwe Cimene Yehova Amapeleka Ndico Malo Anu Acitetezo”​—Gawo 1 (Nehemiya 1:1–6:19)

  • 15:15 Kupanga Ophunzila Pali Pano, Kumatikonzekeletsa Kukapanga Ophunzila m’Dziko Latsopano (Yesaya 11:9; Machitidwe 24:15)

  • 15:50 Nyimbo Na. 140 na Pemphelo Lothela

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani