Tsiku Loyamba
“Tiwonjezeleni cikhulupililo”—Luka 17:5
M’MAŴA
- 9:20 Vidiyo ya Nyimbo 
- 9:30 Nyimbo Na. 5 na Pemphelo 
- 9:40 NKHANI YA CHEYAMANI: Kodi Cikhulupililo N’camphamvu Motani? (Mateyu 17:19, 20; Aheberi 11:1) 
- 10:10 YOSIYILANA: Cifukwa Cake Timakhulupilila . . . - • Kuti Mulungu Aliko (Aefeso 2:1, 12; Aheberi 11:3) 
- • Mawu a Mulungu (Yesaya 46:10) 
- • Miyezo ya Mulungu ya Makhalidwe Abwino (Yesaya 48:17) 
- • Cikondi ca Mulungu (Yohane 6:44) 
 
- 11:05 Nyimbo Na. 37 na Zilengezo 
- 11:15 KUŴELENGA BAIBO MONGA SEŴELO: Nowa—Cikhulupililo Cinamusonkhezela Kumvela Mulungu (Genesis 6:1–8:22; 9:8-16) 
- 11:45 ‘Khalani ndi Cikhulupililo, Osakayika’ (Mateyu 21:21, 22) 
- 12:15 Nyimbo Na. 118 na Kupumula 
MASANA
- 13:35 Vidiyo ya Nyimbo 
- 13:45 Nyimbo Na. 2 
- 13:50 YOSIYILANA: Yang’anani Cilengedwe Kuti Mulimbitse Cikhulupililo Canu - • Nyenyezi (Yesaya 40:26) 
- • Nyanja Zamcele (Salimo 93:4) 
- • Nkhalango (Salimo 37:10, 11, 29) 
- • Mphepo na Madzi (Salimo 147:17, 18) 
- • Zolengedwa za m’Nyanja (Salimo 104:27, 28) 
- • Matupi Athu (Yesaya 33:24) 
 
- 14:50 Nyimbo Na. 148 na Zilengezo 
- 15:00 Nchito Zamphamvu za Yehova Zimalimbitsa Cikhulupililo (Yesaya 43:10; Aheberi 11:32-35) 
- 15:20 YOSIYILANA: Tengelani Citsanzo ca Anthu a Cikhulupililo, Osati Opanda Cikhulupililo - • Abele, Osati Kaini (Aheberi 11:4) 
- • Inoki, Osati Lameki (Aheberi 11:5) 
- • Nowa, Osati Anthu a m’Nthawi Yake (Aheberi 11:7) 
- • Mose, Osati Farao (Aheberi 11:24-26) 
- • Ophunzila a Yesu, Osati Afarisi (Machitidwe 5:29) 
 
- 16:15 “Pitilizani Kudziyesa Kuti Muone Ngati Mukadali Olimba m’Cikhulupililo”—Motani? (2 Akorinto 13:5, 11) 
- 16:50 Nyimbo Na. 119 na Pemphelo