LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • CA-brpgm21 tsa. 4
  • Pezani Mayankho pa Mafunso Aya

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pezani Mayankho pa Mafunso Aya
  • 2020-2021 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woimila Nthambi
  • Nkhani Zofanana
  • Pezani Mayankho pa Mafunso Aya
    2020-2021 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woyang’anila Dela
  • Cimwemwe Khalidwe Locokela kwa Mulungu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Pezani Mayankho pa Mafunso Aya
    2023-2024 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woimila Nthambi
  • Pezani Mayankho pa Mafunso Aya
    2019-2020 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woimila Nthambi
Onaninso Zina
2020-2021 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woimila Nthambi
CA-brpgm21 tsa. 4

Pezani Mayankho Pa Mafunso Aya:

  1. 1. Ni zinthu zitatu ziti zocokela kwa Yehova zimene zimatipatsa cimwemwe? (Sal. 32:1-10)

  2. 2. Kodi tingakhale bwanji acimwemwe pali pano? (Sal. 5:11, 12; 91:14)

  3. 3. Kodi tingakhale bwanji acimwemwe mu ulaliki olo kuti tikukumana na zovuta? (Mac. 13:50-52; Aroma 5:3-5)

  4. 4. Kodi tingapewe bwanji ‘kulemedwa’ na kutaya cimwemwe cathu? (Luka 21:34)

  5. 5. Kodi Yehova amatipangitsa bwanji kukhala acimwemwe?(Sal. 92:4, 5)

  6. 6. N’ciani cidzatithandiza kuika Yehova patsogolo pathu nthawi zonse? (Aroma 1:20; Deut. 6:6-9; Afil. 4:6; Sal. 16:3)

© 2020 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani