LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • CO-pgm24 masa. 2-3
  • Tsiku Loyamba

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tsiku Loyamba
  • Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2024
  • Nkhani Zofanana
  • Tsiku Laciŵili
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2024
  • Tsiku Lacitatu
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2024
  • Tsiku Laciŵili
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2021
  • Tsiku Lacitatu
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2021
Onaninso Zina
Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2024
CO-pgm24 masa. 2-3
Zithunzi: Zimene zili mu pulogilamu ya Tsiku Loyamba. 1. Mngelo akulankhula na Zekariya m’nyumba yopatulika ya kacisi. Zekariya wacita mantha. 2. Mariya, namwali wa Ciyuda, akuoneka wodabwa. 3. Yosefe na Mariya akuyenda na bulu. Mariya wanyamula Yesu.

Tsiku Loyamba

“Uthenga wabwino wa cimwemwe cacikulu cimene anthu onse adzakhale naco”​—Luka 2:10

M’maŵa

  • 8:20 Vidiyo ya Nyimbo

  • 8:30 Nyimbo Na. 150 na Pemphelo

  • 8:40 NKHANI YA CHEYAMANI: N’cifukwa Ciyani Tikufunikila Uthenga Wabwino?(1 Akorinto 9:16; 1 Timoteyo 1:12)

  • 9:10 SEŴELO LALIKULU LA M’BAIBO:

    Uthenga Wabwino Wolalikidwa na Yesu: Mbali 1

    Kuwala Kwenikweni kwa Dziko—Gawo Loyamba (Mateyu 1:​18-25; Luka 1:​1-80; Yohane 1:​1-5)

  • 9:45 Nyimbo Na. 96 na Zilengezo

  • 9:55 YOSIYILANA: “Anatsogoleledwa na Mzimu Woyela”

    • • Mateyu (2 Petulo 1:21)

    • • Maliko (Maliko 10:21)

    • • Luka (Luka 1:​1-4)

    • • Yohane (Yohane 20:31)

  • 11:10 Nyimbo Na. 110 na Kupumula

Masana

  • 12:35 Vidiyo ya Nyimbo

  • 12:45 Nyimbo Na. 117

  • 12:50 YOSIYILANA: Khulupililani Coonadi Conena za Yesu

    • • Mawu (Yohane 1:1; Afilipi 2:​8-11)

    • • Dzina Lake (Machitidwe 4:12)

    • • Kubadwa Kwake (Mateyu 2:​1, 2, 7-12, 16)

  • 13:30 Nyimbo Na. 99 na Zilengezo

  • 13:40 YOSIYILANA: Zimene Tingaphunzile Tikadziŵa Bwino Kumene Yesu Anakulila

    • • Zacilengedwe Zopezeka ku Delalo (Deuteronomo 8:7)

    • • Nyama (Luka 2:​8, 24)

    • • Zakudya (Luka 11:3; 1 Akorinto 10:31)

    • • Umoyo wa Panyumba (Afilipi 1:10)

    • • Anthu a Kudelalo (Deuteronomo 22:4)

    • • Maphunzilo (Deuteronomo 6:​6, 7)

    • • Kulambila (Deuteronomo 16:​15, 16)

  • 15:15 Kodi “Uthenga Wabwino” ni Wosatha M’lingalilo Lotani? (Chivumbulutso 14:​6, 7)

  • 15:50 Nyimbo Na. 66 na Pemphelo Lothela

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani