LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • CA-brpgm26 tsa. 4
  • Pezani Mayankho pa Mafunso Aya

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pezani Mayankho pa Mafunso Aya
  • 2025-2026 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woimila Nthambi
  • Nkhani Zofanana
  • Pezani Mayankho pa Mafunso Aya
    2025-2026 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woyang’anila Dela
  • Zisankho Zimene Zimaonetsa Kuti Timadalila Yehova
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Lembani Mmene Mwapitila Patsogolo
    Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa
  • Muzivomeleza Kuti Pali Zimene Simudziwa
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2025
Onaninso Zina
2025-2026 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woimila Nthambi
CA-brpgm26 tsa. 4

Pezani Mayankho pa Mafunso Aya:

  1. 1. Tingaonetse motani kuti ‘timamvera zimene mzimu ukunena’? (Chiv. 1:​3, 10, 11; 3:19)

  2. 2. N’ciyani cingatithandize kupitiriza kugwira nchito mwakhama komanso kupirira? (Chiv. 2:4)

  3. 3. Kodi tingacite ciani kuti tikonzekere kupirira cizunzo molimba mtima? (Miy. 29:25; Chiv. 2:​10, 11)

  4. 4. Kodi tingacite ciani kuti tipewe kukana kuti timakhulupirira Yesu? (Chiv. 2:​12-16)

  5. 5. Kodi tingacite ciani kuti tipitirize kugwira mwamphamvu zinthu zimene tiri nazo? (Chiv. 2:​24, 25; 3:​1-3, 7, 8, 10, 11)

  6. 6. N’ciani cingatithandize kukhalabe odzipereka? (Chiv. 3:​14-19; Mat. 6:​25-27, 31-33)

© 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

CA-brpgm26-CIN

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani