LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • wp20 na. 2 tsa. 16
  • Kodi Ufumu wa Mulungu N’ciani?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Ufumu wa Mulungu N’ciani?
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Coonadi Ponena za Ufumu wa Mulungu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2020
  • Kodi Baibulo Imakamba Ciani?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2016
  • “Ufumu Wanu Udze”—Pemphelo Limene Anthu Ambili Amapeleka
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2020
  • Kuyankha Mafunso a m’Baibulo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
Onaninso Zina
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2020
wp20 na. 2 tsa. 16

Kodi Ufumu Wa Mulungu N’ciani?

Munthu aŵelenga Baibo ndipo wakhala pa benchi kutsogolo kwa nyumba ina ya boma.

Anthu ambili amapemphela kuti Ufumu wa Mulungu ubwele. Koma kodi munadzifunsapo kuti Ufumu wa Mulungu n’ciani? Nanga udzacita ciani?

ONANI ZIMENE BAIBO IMAKAMBA:

  • Kodi Ufumu wa Mulungu N’ciani?

    Ni boma la kumwamba limene wolamulila wake ni Yesu Khristu monga Mfumu.—Yesaya 9:6, 7; Mateyu 5:3; Luka 1:31-33.

  • Kodi Ufumu wa Mulungu udzacita ciani?

    Udzacotsapo zoipa zonse na kubweletsa mtendele wamuyaya kwa anthu padziko lapansi.—Danieli 2:44; Mateyu 6:10.

  • Kodi kufuna-funa Ufumu coyamba kumatanthauza ciani?

    Kumatanthauza kucilikiza Ufumu wa Mulungu, na kukhulupilila kuti iwo wokha ndiwo udzakonza zinthu padziko lapansi kuti zikhale mmene Mulungu amafunila.—Mateyu 6:33; 13:44.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani