LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 11/14 tsa. 3
  • “Sindimupezanso Panyumba!”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Sindimupezanso Panyumba!”
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Nkhani Zofanana
  • Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kulalikila Pafoni
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kuyala Maziko a Ulendo Wobwelelako
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Danga la Mafunso
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kupanga Ulendo Wobwelelako
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Onaninso Zina
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 11/14 tsa. 3

“Sindimupezanso Panyumba!”

Kodi munalankhulapo mau amenewa ponena za munthu amene anaonetsa cidwi? Kuthilila mbeu ya coonadi imene munafesa kumakhala kovuta ngati munthuyo simum’peza. (1 Akor. 3:6) Nthawi zina, ofalitsa ozoloŵela ulaliki amalembela kalata munthu amene samupeza panyumba kapena amamulembela kapepala n’kukasiya munsi mwa citseko. Ofalitsa ena akaona kuti zidzakhala zovuta kupezanso munthuyo panyumba, amam’pempha nambala ya foni. Mungalembe ulendo wobweleza pamene mwafikila munthu amene munalalikila, kaya mocita kumulembela kalata, imelo, uthenga pafoni, kumulembela kapepala kapena kumutumila foni. Kucita zimenezi kungakulitse cidwi ca munthuyo ngakhale kuti sapezekapezeka panyumba.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani