LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 April tsa. 1
  • Maulaliki Acitsanzo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Maulaliki Acitsanzo
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Tumitu
  • Nkhani Zofanana
  • GALAMUKANI!
  • GALAMUKANI!
  • Zimene Baibo Imaphunzitsa
  • LEMBANI ULALIKI WANU
  • Maulaliki Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Maulaliki Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Maulaliki a Citsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Maulaliki a Citsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 April tsa. 1
Amene anapezeka pa Msonkhano wa Maiko wa Mboni za Yehova ku New Jersey, U.S.A.

Abale ndi alongo pa msonkhano wa maiko mu 2014 ku New Jersey, U.S.A.

Maulaliki Acitsanzo

GALAMUKANI!

Magazini a Galamukani! Na. 2 2016 | Is the Bible Just a Good Book?

Kugaŵila Cofalitsa: Ndakubweletselani Galamukani! iyi yatsopano.

Funso: Onani funso ili patsamba 2. Kodi muganiza bwanji?

Lemba: Luka 7:35

Nkhani iyi ifotokoza mmene mfundo imeneyi ilili yoona ponena za Baibulo.

GALAMUKANI!

Funso: Kodi muvomeleza kuti mau awa ndi ofunika kuwatsatila?

Lemba: Mat. 6:34

Kugaŵila Cofalitsa: [Pezani nkhani yakuti “Lingaliro la Baibulo—Nkhawa.”] Nkhani ino ionetsa mmene Baibulo lingatithandizile kulimbana ndi nkhawa.

Zimene Baibo Imaphunzitsa

Zimene Baibo Imaphunzitsa m’Ceniceni

Funso: Anthu amene amakhulupilila Mulungu amafuna kumuyandikila. Kodi mudziŵa kuti Baibulo limatilimbikitsa kuyandikila Mulungu?

Lemba: Yak. 4:8a

Kugaŵila Cofalitsa: Buku ili linapangidwa kuti litithandize kudziŵa zambili za Mulungu mwa kuseŵenzetsa Baibulo. [Fotokozani mfundo za m’nkhani 1 m’buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa.]

LEMBANI ULALIKI WANU

Onani maulaliki acitsanzo amene asonyezedwa kale kuti akuthandizeni kulemba ulaliki wanu.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani