LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 July tsa. 5
  • Anthu a Yehova ni Okangalika pa Kulambila Koona

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Anthu a Yehova ni Okangalika pa Kulambila Koona
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • ‘Zimenezo Uziphunzitse kwa Amuna Okhulupilika’
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Mafunso Ocokela kwa Oŵelenga
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2024
  • M’Nyengo Ino ya Cikumbutso, Kodi Mudzatengela Kudzipeleka kwa Yehova ndi Yesu?
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Muziyamikila Mphamvu za Acinyamata
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 July tsa. 5

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MASALIMO 69-73

Anthu a Yehova ni Okangalika pa Kulambila Koona

Cangu cathu pa kulambila koona cizionekela

69:9

  • Davide anali wacangu potumikila Yehova umoyo wake wonse

  • Davide sanalole munthu aliyense kutsutsana ndi Yehova kapena kutonza dzina la Mulungu

Davide akumana ndi Goliyati ndi msilikali wake womunyamulila zida zankhondo

Acikulile angathandize acicepele kukhala okangalika

Davide aŵelenga mpukutu ndi wacicepele

71:17, 18

  • Wolemba salimo imeneyi amene mwina ndi Davide, anaonetsa kuti anali wofunitsitsa kulimbikitsa mbadwo wotsatila

  • Makolo ndi Akhiristu ofikapo mwauzimu angaphunzitse acicepele

Tikakhala acangu timauzako ena zimene Ufumu wa Mulungu udzacitila anthu

72:3, 12, 14, 16-19

  • Amuna aŵili apatsana moni

    Vesi 3—Anthu onse adzakhala pa mtendele

  • Munthu wosauka athandizidwa

    Vesi 12—Osauka adzalanditsidwa

  • Mfuti yatyoledwa zidutswa-zidutswa

    Vesi 14—Ciwawa cidzatha

  • Aliyense adzakhala na cakudya cokwanila

    Vesi 16—Aliyense adzakhala ndi cakudya ca mwana alilenji

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani