LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 March tsa. 4
  • Anthu Angapambane Kokha Ngati Atsogozedwa na Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Anthu Angapambane Kokha Ngati Atsogozedwa na Yehova
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Zamkatimu
    Galamuka!—2022
  • “Ine Ndili ndi Iwe Kuti Ndikulanditse”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • M’kope Ino ya Galamuka!
    Galamuka!—2022
  • Khalani Wolimba Mtima Monga Yeremiya
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 March tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YEREMIYA 8-11

Anthu Angapambane Kokha Ngati Atsogozedwa na Yehova

Anthu sangakwanitse kudzilamulila, ndipo si oyenelela kutelo

10:21-23

  • Cifukwa cakuti abusa auzimu a Aisiraeli sanali kufunsila kwa Yehova, anthu anamwazikana

    Abusa a mu Isiraeli afunsila kwa milungu yonama; Yerusalemu awonongedwa
  • Koma amene anatsatila citsogozo ca Yehova anali kukhala mwa mtendele mwa cimwemwe, ndipo zinthu zinali kuwayendela bwino

    Mwiisiraeli aŵelenga cilamulo ca Mulungu ndipo ni wosangalala, wacimwemwe ndiponso zinthu zikumuyendela bwino na banja lake
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani