LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 May tsa. 2
  • Cizindikilo Cakuti Isiraeli Adzabwezeletsedwa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Cizindikilo Cakuti Isiraeli Adzabwezeletsedwa
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Ubwino—Kodi tingalikulitse bwanji khalidwe limeneli?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • Khalani Wolimba Mtima Monga Yeremiya
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 May tsa. 2

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YEREMIYA 32-34

Cizindikilo Cakuti Isiraeli Adzabwezeletsedwa

Yopulinta

32:9-14

  • Yeremiya anatsatila ndondomeko pogula munda

    Pogula munda, Yeremiya anaona ndalama zimene anali nazo, ndiyeno analemba zonse pa colembapo na kusungila m’ciwiya cadothi

33:10, 11

  • Yehova anaonetsa ubwino wake mwa kulonjeza kuti otengeledwa ku ukapolo amene anamvela malangizo ake adzawakhululukila na kuwabweza ku Isiraeli

    Mapu yoonetsa Yerusalemu ndi tawuni ya Anatoti kwawo kwa Yeremiya

Kodi Yehova waonetsa bwanji ubwino wake kwa imwe?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani