LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 June tsa. 1
  • Maulaliki a Citsanzo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Maulaliki a Citsanzo
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Tumitu
  • Nkhani Zofanana
  • GALAMUKANI!
  • PHUNZITSANI COONADI
  • KODI COFUNIKA N’CIANI KUTI BANJA LIKHALE LAMTENDELE?
  • KONZANI ULALIKI WANU
  • Maulaliki a Citsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Maulaliki a Citsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Maulaliki a Citsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Maulaliki Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 June tsa. 1
Mlongo aŵelenga Baibo na kusinkha-sinkha

Kupatula nthawi yophunzila Baibo na kusinkha-sinkha

Maulaliki a Citsanzo

GALAMUKANI!

Galamukani! Na. 3 2017 | Kodi Baibulo ndi Lochokeradi Kwa Mulungu?

Funso: Kodi Baibo ni yocokeladi kwa Mulungu? Kapena ni buku lodzala na maganizo a anthu?

Lemba: 2 Tim. 3:16

Cogaŵila: Galamukani! ino ifotokoza maumboni atatu oonetsa kuti Baibo ni yocokeladi kwa Mulungu.

PHUNZITSANI COONADI

Baibo yotsegula

Funso: Kodi mphatso ya moyo tiyenela kuiona bwanji?

Lemba: Chiv. 4:11

Coonadi: Popeza moyo ni mphatso yocokela kwa Mulungu, timaulemekeza. Timayesetsa kupewa ngozi, ndipo sitingayese kupha munthu mwadala. Timalemekeza kwambili mphatso imeneyi ya moyo.

KODI COFUNIKA N’CIANI KUTI BANJA LIKHALE LAMTENDELE?

Kodi Cofunika N’ciani Kuti Banja Likhale Lamtendele?

Funso: Onani funso limene lili pa kapepa aka kauthenga na mayankho amene alipo. Imwe muganiza bwanji?

Lemba: Luka 11:28

Cogaŵila: Kapepa kauthenga aka kafotokoza phindu limene mungapeze ngati mutsatila malangizo a m’Baibo pabanja lanu ndiponso cifukwa cake tiyenela kukhulupilila zimene Baibo imakamba.

KONZANI ULALIKI WANU

Funso:

Lemba:

Cogaŵila:

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani