LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 July tsa. 5
  • Kodi Yehova Akatikhululukila Macimo, Amawakumbukilanso?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Yehova Akatikhululukila Macimo, Amawakumbukilanso?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Mmene Kukhululuka kwa Yehova Kumatipindulila
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2025
  • Muzikhulupirira Kuti Yehova Anakukhululukirani
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2025
  • Yehova Ni Wokonzeka Kukhululuka
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Kuyankha Mafunso a M’Baibo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 July tsa. 5

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | EZEKIELI 18-20

Kodi Yehova Akatikhululukila Macimo, Amawakumbukilanso?

18:21, 22

  • Yehova akatikhululukila macimo, samadzatiimbanso mlandu cifukwa ca macimowo.

Zitsanzo za anthu a m’Baibo zimatithandiza kukhulupilila kuti Yehova amatikhululukiladi.

Mfumu Davide

Mfumu Davide akumva cisoni cifukwa ca chimo lake
  • N’ciani cimene analakwa?

  • N’cifukwa ciani anam’khululukila?

  • Kodi Yehova anamuonetsa bwanji kuti anam’khululukila?

Mfumu Manase

Mfumu Manase acondelela Yehova kuti amukhululukile
  • N’ciani cimene analakwa?

  • N’cifukwa ciani anam’khululukila?

  • Kodi Yehova anamuonetsa bwanji kuti anam’khululukila?

Mtumwi Petulo

Mtumwi Petulo akumva cisoni pambuyo pokana Yesu
  • N’ciani cimene analakwa?

  • N’cifukwa ciani anam’khululukila?

  • Kodi Yehova anamuonetsa bwanji kuti anam’khululukila?

Ningam’tengele bwanji Yehova pa nkhani yokhululuka?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani