LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 August tsa. 4
  • Kulitsani Makhalidwe Aumulungu—Kulimba Mtima

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kulitsani Makhalidwe Aumulungu—Kulimba Mtima
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Kukhala Wolimba Mtima Sikovuta
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • ‘Limba Mtima, Ugwile Nchito Mwamphamvu’
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Nilimbitseni Mtima
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Cilimikani Pamene Mapeto Ayandikila
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 August tsa. 4

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Kulitsani Makhalidwe Aumulungu—Kulimba Mtima

CIFUKWA CAKE N’KOFUNIKA:

  • Kulalikila kumafuna kulimba mtima. —Mac. 5:27-29, 41, 42

  • Cisautso cacikulu cidzatiyesa pa kulimba mtima kwathu.—Mat. 24:15-21

  • Kuopa anthu kumabweletsa mavuto. —Yer. 38:17-20; 39:4-7

MMENE TINGAKULITSILE KULIMBA MTIMA:

  • Sinkha-sinkhani za mmene Yehova anapulumutsila anthu.—Eks. 14:13

  • Pemphani Mulungu kuti mukhale olimba mtima.—Mac. 4:29, 31

  • Dalilani Yehova.—Sal. 118:6

Abale aŵili alimbikitsa m’bale wina kuti apitile pamodzi mu ulaliki wapoyela

Ni mantha a ciani mu utumiki wanga amene niyenela kugonjetsa?

TAMBANI VIDIYO YAKUTI MUZIPEWA ZINTHU ZIMENE ZINGAKULEPHELETSENI KUKHALA WOKHULUPILIKA —KUOPA ANTHU, NDIYENO YANKHANI MAFUNSO AYA:

  • N’cifukwa ninji kulimba mtima n’kofunika mu utumiki?

  • Kodi pa Miyambo 29:25 pali zinthu ziŵili ziti zosiyana?

  • N’cifukwa ciani tifunika kukulitsa khalidwe la kulimba mtima pali pano?

CITSANZO CA M’BAIBO COFUNIKA KUGANIZILA:

Ezekieli anauzidwa kuti nchito yake ya uneneli idzakhala yovuta.—Ezek. 2:3-7; 33:7-9.

Dzifunseni kuti, ‘Ningatengele bwanji kulimba mtima kwa Ezekieli?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani