LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 September tsa. 2
  • Ǹ’cifukwa Ciani Kulambila Koyela Kuli Kofunika?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ǹ’cifukwa Ciani Kulambila Koyela Kuli Kofunika?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Kubwezeletsa Kulambila Koyela
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Yehova Amafuna Anthu Ake Kukhala Oyela
    Mmene Tingakhalilebe mu Cikondi ca Mulungu
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 September tsa. 2

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Ǹ’cifukwa Ciani Kulambila Koyela Kuli Kofunika?

Ayuda amene anali ku ukapolo analimbikitsidwa na masomphenya a kacisi amene Ezekieli anaona. Masomphenyawo anawapatsa ciyembekezo cakuti kulambila koyela kudzabwezeletsedwa. M’masiku otsiliza ano, kulambila koyela ‘kwakhazikika pamwamba pa nsonga za mapili,’ ndipo ise tili pakati pa anthu amene akhamukila ku phili limenelo. (Yes. 2:2) Kodi mumayamikila mwayi wodziŵa Yehova na kum’tumikila?

MADALITSO A KULAMBILA KOYELA:

  • M’bale aŵelenga Baibo

    Cakudya cauzimu coculuka cimene cimapeleka mayankho pa mafunso ofunika ngako onena za umoyo. Cimatithandizanso kukhala na makhalidwe abwino ndi ciyembekezo cotsimikizika.—Yes. 48:17, 18; 65:13; Aroma 15:4

  • Ubale wa padziko lonse.—Sal. 133:1; Yoh. 13:35

  • Mwayi wokhala anchito anzake a Mulungu pa nchito yokhutilitsa.—Mac. 20:35; 1 Akor. 3:9

  • “Mtendele wa Mulungu” umene umatilimbitsa pa nthawi ya mavuto.—Afil. 4:6, 7

  • Cikumbumtima coyela.—2 Tim. 1:3

  • “Ubwenzi wolimba ndi Yehova.”—Sal. 25:14.

Ningaonetse bwanji kuti nimaona kulambila koyela kukhala kofunika ngako?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani