LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 May tsa. 7
  • Pewani Msampha wa Kuopa Anthu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pewani Msampha wa Kuopa Anthu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • “Ndakupatsani Citsanzo”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Yesu Amakonda Tuŵana
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • “Simuli Mbali ya Dzikoli”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Kulitsani Makhalidwe Aumulungu—Kulimba Mtima
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 May tsa. 7

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MALIKO 13-14

Pewani Msampha wa Kuopa Anthu

N’cifukwa ciani atumwi anathaŵa zinthu zitavuta?

14:29, 31

  • Anadzidalila kwambili. Ndipo Petulo anafika podziona kuti adzakhulupilika ngako kwa Yesu kuposa atumwi ena onse

    Petulo akana Yesu

14:32, 37-41

  • Analephela kukhalabe maso na kupemphela

    Atumwi akugona pamene Yesu apemphela

Yesu ataukitsidwa, n’ciani cinathandiza atumwi kupewa msampha wa kuopa anthu na kupitiliza kulalikila olo kuti anali kutsutsidwa?

13:9-13

  • Anamvela macenjezo a Yesu, ndipo anali okonzeka kupilila citsutso na cizunzo

  • Anadalila Yehova mwa kupemphela.—Mac. 4:24, 29

    Petulo na Yohane aimilila m’Khoti Lalikulu la Ayuda

N’zocitika ziti zimene zingafune kuti tikhale olimba mtima?

Mzimayi wa Mboni ali pabedi m’cipatala ndipo akukamba na dokota wake; kamnyamata ka Mboni kali m’kilasi ndipo sikakucitako saliyuti mbendela; wa Mboni walandila ciitanilo ca ku pati
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani