LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 October tsa. 5
  • “Ndakupatsani Citsanzo”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Ndakupatsani Citsanzo”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Amaona Atumiki Ake Odzicepetsa Kukhala Amtengo Wapatali
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • Muziyesetsa Kukhala Mwamtendele na Ena
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Pewani Msampha wa Kuopa Anthu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • “Cilimikani ndi Kuona Cipulumutso ca Yehova”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 October tsa. 5
Yesu asambika mapazi a atumwi ake

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YOHANE 13-14

“Ndakupatsani Citsanzo”

13:5, 12-15

Mwa kusambika mapazi a atumwi ake, Yesu anawaphunzitsa kuti afunika kukhala odzicepetsa komanso okonzeka kugwila nchito zotsika potumikila ena.

Ningaonetse bwanji kuti ndine wodzicepetsa pamene . . .

  • Alongo aŵili asemphana maganizo

    tayambana kapena kusemphana maganizo na wina?

  • M’bale akupeleka uphungu kwa m’bale wina

    wina akunilangiza kapena kunipatsa uphungu?

  • Abale na alongo akuyeletsa Nyumba ya Ufumu

    alengeza kuti kuli kuyeletsa na kukonza zinthu pa Nyumba ya Ufumu?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani