LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 August tsa. 2
  • “Cilimikani ndi Kuona Cipulumutso ca Yehova”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Cilimikani ndi Kuona Cipulumutso ca Yehova”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Wamphamvuzonse Koma Woganizila Ena
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • “Ndakupatsani Citsanzo”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • “Tsopano Uona Zimene Ndicite kwa Farao”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Mwambo wa Pasika—Zimene Umatanthauza kwa Akhristu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 August tsa. 2
Aisiraeli akuwoloka Nyanja Yofiila pa nthaka youma. Moto woima njo ngati cipilala ukuwaunikila.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EKSODO 13-14

“Cilimikani ndi Kuona Cipulumutso ca Yehova”

14:13, 14, 21, 22, 26-28

Yehova ni mpulumutsi amene amaganizila ena. Kodi anaonetsa bwanji kuwaganizila Aisiraeli pamene anali kutuluka mu Iguputo?

  • Anawayendetsa mwadongosolo.—Eks. 13:18

  • Anawatsogolela na kuwateteza.—Eks. 14:19, 20

  • Anapulumutsa anthu ake onse, kuyambila ana mpaka okalamba.—Eks. 14:29, 30

Kodi mungakhale otsimikiza za ciani pamene cisautso cacikulu cikuyandikila?—Yes. 30:15

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani