LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 July tsa. 6
  • Mwambo wa Pasika—Zimene Umatanthauza kwa Akhristu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mwambo wa Pasika—Zimene Umatanthauza kwa Akhristu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Mlili wa Namba 10
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • ‘Ici Cidzakhala Cikumbutso Kwa Inu’
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
  • Pasika na Cikumbutso—Kulingana na Kusiyana Kwake
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • “Cilimikani ndi Kuona Cipulumutso ca Yehova”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 July tsa. 6
Banja la laciisiraeli laimilila ndipo likudya cakudya ca pasika lisanatuluke mu Iguputo.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EKSODO 12

Mwambo wa Pasika—Zimene Umatanthauza kwa Akhristu

12:5-7, 12, 13, 24-27

Kuti Aisiraeli apewe kuvulazidwa na mlili wa namba 10, iwo anafunika kumvela malangizo. (Eks. 12:28) Usiku, pa Nisani 14, mabanja anasonkhana pamodzi m’nyumba zawo. Iwo anafunika kupha nkhosa kapena mbuzi yopanda cilema, yamphongo, ya caka cimodzi. Magazi ake anafunika kuwawaza pa mafelemu a nyumba zawo, komanso pamwamba pa khomo. Ndiyeno anafunika kuwocha nyama yonse na kuidya mofulumila. Munthu aliyense sanafunike kutuluka m’nyumba yake mpaka m’mawa.—Eks. 12:9-11, 22

Kodi kumvela kumatiteteza m’njila zina ziti masiku ano?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani