LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 November tsa. 5
  • Mapindu a pa Dziko Lonse a Ulaliki wa pa Kasitandi

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mapindu a pa Dziko Lonse a Ulaliki wa pa Kasitandi
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Zonsezi Zinatheka Cifukwa ca Kumwetulila!
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Tumasitandi twa Ulaliki Tothandiza Pocitila “Umboni ku Mitundu Yonse”
    Mmene Zopeleka Zanu Zimagwilila Nchito
  • Mmene Mungacitile Ulaliki Pogwilitsila Nchito Thebulo Kapena Shelufu ya Zofalitsa
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 November tsa. 5
Abale aŵili akucita ulaliki wapoyela wa pa kasitandi

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Mapindu a pa Dziko Lonse a Ulaliki wa pa Kasitandi

Kulingana na Machitidwe caputa 5, Akhristu a m’nthawi ya atumwi anapita ku kacisi, malo amene kunali kupezeka anthu ambili kuti akalalikile uthenga wabwino. (Mac. 5:19-21, 42) Masiku ano, taona zotulukapo zabwino za ulaliki wapoyela wa tumasitandi.

TAMBITSANI VIDIYO YAKUTI MAPINDU A ULALIKI WA KASITANDI, NDIYENO YANKHANI MAFUNSO AYA:

  • Mi Jung You akucita ulaliki wapoyela wa pa kasitandi; Jacob Salomé; Mlongo Annies na mwamuna wake akucita ulaliki wapoyela wa pa kasitandi

    Kodi ulaliki wa pa kasitandi unayamba liti? Nanga unayamba bwanji?

  • Kodi kuseŵenzetsa kasitandi kuli na ubwino wanji kuposa kuseŵenzetsa thebulo?

  • Kodi cocitika ca mlongo Mi Jung You citiphunzitsa ciani?

  • Kodi cocitika ca m’bale Jacob Salomé cionetsa bwanji kufunika kwa ulaliki wa pa kasitandi?

  • Kodi cocitika ca mlongo Annies na mwamuna wake citiphunzitsa ciani pankhani ya mmene tingacitile ulaliki wa pa kasitandi mogwila mtima?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani