LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 March tsa. 6
  • “Cofufumitsa Cacing’ono Cimafufumitsa Mtanda Wonse”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Cofufumitsa Cacing’ono Cimafufumitsa Mtanda Wonse”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Cifukwa Cake Kucotsa Munthu Mumpingo Ndi Makonzedwe Acikondi
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Munthu Amene Timakonda Akasiya Yehova
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Timaonetsa Cikondi Ngati Ticita Zinthu Mogwilizana na Cilango ca Yehova
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Kodi Tiyenela Kucita Bwanji ndi Munthu Wocotsedwa?
    “Khalanibe m’Cikondi ca Mulungu”
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 March tsa. 6
Munthu wocotsedwa acoka mu Nyumba ya Ufumu pambuyo pa misonkhano; ayang’ana abale na alongo amene akuceza

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 1 AKORINTO 4-6

“Cofufumitsa Cacing’ono Cimafufumitsa Mtanda Wonse”

5:1, 2, 5-11, 13

N’cifukwa ciani tingakambe kuti kucotsa munthu mumpingo ni makonzedwe acikondi, popeza cimapweteka mtima?

Kucotsa munthu mu mpingo kumaonetsa kuti . . .

  • timakonda Yehova, komanso timalemekeza dzina lake.—1 Pet. 1:15, 16

  • timakonda mpingo pouteteza ku makhalidwe oipa.—1 Akor. 5:6

  • timakonda wocimwayo cifukwa kumamuthandiza kuzindikila colakwa cake.—Aheb. 12:11

Kodi tingalithandize bwanji banja lacikhristu limene lili na munthu wocotsedwa?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani