LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 August tsa. 2
  • “Mulungu Sanatipatse Mzimu Wamantha”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Mulungu Sanatipatse Mzimu Wamantha”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • “Simuli Mbali ya Dzikoli”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Zamkatimu
    Galamuka!—2022
  • Timoteyo Anafunitsitsa Kuthandiza Anthu
    Phunzitsani Ana Anu
  • “Mwana Wanga Wokondedwa ndi Wokhulupilika mwa Ambuye”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2016
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 August tsa. 2

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 2 TIMOTEYO 1-4

“Mulungu Sanatipatse Mzimu Wamantha”

1:7, 8

Timoteyo aŵelenga mpukutu wocokela kwa mtumwi Paulo

Mawu ouzilidwa amene mtumwi Paulo anauza Timoteyo angatilimbikitse. M’malo mocita manyazi na uthenga wabwino, tingalankhule molimba mtima za cikhulupililo cathu, ngakhale kuti nthawi zina zingacititse kuti ‘timve zowawa.’

Ni pa zocitika ziti pamene nifunika kukhala wolimba mtima?

Mlongo wacicepele akulongoza anzake a m’kilasi na atica bulosha yakuti Origin of Life; Mlongo akukana kuika zokongoletsela ku mtengo wa Khrisimasi umene uli ku nchito kwake; m’bale akulalikila ku nchito kwake
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani