LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 October tsa. 4
  • “Mapeto a Zinthu Zonse Ayandikila”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Mapeto a Zinthu Zonse Ayandikila”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Kucelezana ni Khalidwe Lofunika Kwambili
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Mmene Tingalimbikitsile Cikondi Cathu pa Ena
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Gaŵanani ndi Ena “Zabwino” mwa Kukhala Woceleza (Mat. 12:35a)
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Muzikondana Kwambili
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 October tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 1 PETULO 3-5

“Mapeto a Zinthu Zonse Ayandikila”

4:7-9

M’bale wacinyamata wakhala pa mpando wa sofa, ndipo akupemphela

Posacedwa, tiyang’anizana na cisautso cacikulu cimene sicinacitikepo padzikoli. Tingacite ciani kuti tikhalebe okhulupilika lomba mpaka m’tsogolo?

  • Muzipemphela mosalekeza, mwa kuseŵenzetsa mtundu uliwonse wa pemphelo

  • Kulitsani cikondi canu pa abale na alongo, ndipo pitilizani kulimbitsa ubwenzi wanu ndi iwo

  • Muziwaceleza mwacimwemwe

Mwamuna na mkazi wake abweletsa zakudya na zovala kwa tate na ana ake aŵili; Mboni za Yehova zikukonza mtenje pambuyo pa ngozi yacilengedwe

DZIFUNSENI KUTI, ‘Ni njila ziti zimene ningaonetsele kuti ndine wacikondi ndiponso woceleza kwa abale na alongo a m’dela lathu komanso a ku maiko ena?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani