LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 November tsa. 8
  • Mphamvu ya ‘Tumakobili Tuŵili Twatung’ono’

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mphamvu ya ‘Tumakobili Tuŵili Twatung’ono’
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Timayamika Yehova Cifukwa ca Cikondi Canu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Yehova Amakonda Munthu Wopeleka Mokondwela
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • “Okonzeka Kupeleka Mphatso kwa Yehova”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Ni Mphatso Yanji Imene Tingam’patse Yehova?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 November tsa. 8
Mkazi wamasiye akuyang’ana tumakobili twake tuŵili twatung’ono asanatupange copeleka.

UMOYO WACIKHILISITU

Mphamvu ya ‘Tumakobili Tuŵili Twatung’ono’

Copeleka ca mkazi wamasiye cinali cosakwanila ngakhale kugulila cakudya cochipa kwambili. (Onani w08 3/1 peji 12 ndime 1-3.) Komabe, copeleka cake cinaonetsa kuti anali kum’konda kwambili Yehova ndiponso anali kuona kulambila Mulungu kukhala kofunika ngako. Pa cifukwa cimeneci, copelekaco cinali camtengo wapatali kwa Atate wake wakumwamba.—Maliko 12:43.

TAMBANI VIDIYO YAKUTI ‘KUPELEKA MPHATSO KWA YEHOVA,’ KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATILAWA:

  • Zocitika za mu vidiyo yakuti ‘Kupeleka Mphatso Kwa Yehova.’ Ndalama zimene timapeleka zimathandiza pa nchito zomanga za gulu.

    Kodi zopeleka zathu zimathandiza pa nchito monga ziti?

  • Zocitika za mu vidiyo yakuti ‘Kupeleka Mphatso Kwa Yehova.’ Kamtsikana kakupeleka copeleka caufulu m’kabokosi ka zopeleka pa Nyumba ya Ufumu.

    N’cifukwa ciani zopeleka zathu n’zofunika kwambili olo zioneke monga zocepa?

  • Zocitika za mu vidiyo yakuti ‘Kupeleka Mphatso Kwa Yehova.’ Zithunzi: Zopeleka zimacilikiza nchito za Ufumu padziko lonse. 1. Nchito za pa Beteli. 2. Masukulu a zaumulungu. 3. Masoka a zacilengedwe. 4. Nchito zomanga za gulu. 5. Misonkhano yacigawo.

    Tingadziŵe bwanji njila zosiyana-siyana zocitila zopeleka, zimene zilipo m’dela lathu?—Onani bokosi yakuti “Phunzilani Zambili pa Intaneti”

PHUNZILANI ZAMBILI PA INTANETI

Dinizani pa mawu akuti “Donations” amene apezeka munsi mwa peji yoyamba ya JW Laibulali. Malinga na dela limene mukhala, mukaloŵa pamenepo mudzapeza linki yokupelekani ku peji yakuti “Mafunso Ofunsidwa Kaŵili-kaŵili,” imene pali mayankho ku mafunso amene anthu amafunsa kaŵili-kaŵili pankhani ya zopeleka. Nayonso vidiyo yakuti Mmene Mungapelekele Zopeleka pa Intaneti, ili na mfundo zothandiza pa nkhani ya njila zosiyana-siyana zocitila copeleka zimene zilipo.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani