LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb21 May tsa. 3
  • Muzikwanilitsa Malumbilo Anu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Muzikwanilitsa Malumbilo Anu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Nkhani Zofanana
  • ‘Muzikwanilitsa Zimene Mwalonjeza’
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Anthu Okhulupilika Amasunga Malonjezo Awo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2024
  • Zimene Tingaphunzile pa Dongosolo la Msasa wa Aisiraeli
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Utumiki wa Alevi
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
mwb21 May tsa. 3

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Muzikwanilitsa Malumbilo Anu

Aisiraeli anali kupanga malumbilo mwa kufuna kwawo, koma akalumbila anali kufunika kukwanilitsa (Num. 30:2; it-2 1162)

Malumbilo angaphatikizepo kudziletsa ngakhale pa zinthu zimene si zolakwika (Num. 30:3, 4; w17 04 3¶2)

Nkhani ya malumbilo masiku ano imakhala pakati pa Yehova na wolambila aliyense payekha (Num. 30:6-9; w04 8/1 27 ¶3)

Malumbilo aŵili ofunika kwambili amene Mkhristu angapange masiku ano ni lumbilo la kudzipatulila kwa Mulungu komanso la cikwati.

Zithunzi: Anthu akupanga malumbilo. 1. Mtsikana akupemphela. 2. Mwamuna na mkazi wake akuvekana mphete pamwambo wa cikwati cawo.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi nikuyesetsa kukwanilitsa malumbilo amene n’napanga?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani