LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb21 May tsa. 4
  • “Mukapitikitse Anthu Onse a m’Dzikolo”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Mukapitikitse Anthu Onse a m’Dzikolo”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Nkhani Zofanana
  • Mmene Yehova Amatsogolela Anthu Ake
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Mmene Cikhulupililo Cimatithandizila Kukhala Olimba Mtima
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Samalani na Nkhani Zabodza
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Zimene Tingaphunzile pa Dongosolo la Msasa wa Aisiraeli
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
mwb21 May tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

“Mukapitikitse Anthu Onse a m’Dzikolo”

Yehova analamula anthu ake kuti akacotse ciliconse m’Dziko Lolonjezedwa cimene cikanawacititsa kuphwanya malamulo ake (Num. 33:52; w10 8/1 23)

Yehova anawalonjeza kuti adzawadalitsa ngati adzalimbika kulanda dziko lonse la Kanani (Num. 33:53)

Aisiraeli anacenjezedwa kuti adzakumana na mavuto ngati sadzagonjetsa adani awo onse (Num. 33:55, 56; w08 2/15 27 ¶5-6; it-1 404 ¶2)

Kuti tikondweletse Yehova, tiyenela kupewelatu mcitidwe ulionse wodetsedwa, umene ungawononge ubale wathu na iye. (Yak. 1:21) Yehova amatipatsa mphamvu zotithandiza kugonjetsa macitidwe aucimo na kupewa mzimu woipa wa dzikoli.

Acinyamata atatu akucita maseŵela aciwawa a pavidiyo mosangalala.
Wacinyamata akuzima TV.
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani