LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 March tsa. 8
  • Mmene Mungakhalile Bwenzi Labwino

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mmene Mungakhalile Bwenzi Labwino
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Mulungu Akupemphani Kuti Mukhale Mnzake
    Na Imwe Mungakhale Mnzake wa Mulungu!
  • Dzilimbitseni mwa Yehova Mulungu Wanu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Baibo—Buku Limene Limakamba Zenizeni Osati Nthano
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Mukhoza Kukhala Bwenzi la Yehova
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 March tsa. 8

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Mmene Mungakhalile Bwenzi Labwino

Tonthozani na kulimbikitsa bwenzi lanu limene lapsinjika maganizo (1 Sam. 20:1, 2; w19.11 7 ¶18)

Cenjezani bwenzi lanu pakakhala zoopsa (1 Sam. 20:12, 13; w08 2/15 8 ¶7)

Bwenzi lanu likamanenezedwa na ena, muzilikhalila kumbuyo (1 Sam. 20:30-32; w09 10/15 19 ¶11)

Mwamuna na mkazi wake akumvetsela pamene m’bale akuwafotokozela mavuto amene wakumana nawo.

Anthu a Yehova ali na mipata yambili yopezela mabwenzi abwino. Kuti mupeze bwenzi, muyenela kukhala waubwenzi. N’ndani amene mungakonde kupalana naye ubwenzi mumpingo?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani