LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 September tsa. 4
  • Sankhani Mwanzelu Munthu Womanga Naye Banja

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Sankhani Mwanzelu Munthu Womanga Naye Banja
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Mukumbukila?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Thandizani Acinyamata Kuti Apambane
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Yehova Ni Mulungu Woganizila Ena
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • “Ndinamutsutsa Pamasom’pamaso”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 September tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Sankhani Mwanzelu Munthu Womanga Naye Banja

Solomo anacita zinthu mopanda nzelu mwa kukwatila akazi opembedza mafano (1 Maf. 11:1, 2; w18.07 18 ¶7)

M’kupita kwa nthawi, akazi amene Solomo anakwatila anapatutsa mtima wake na kuucotsa kwa Yehova (1 Maf. 11:3-6; w19.01 15 ¶6)

Yehova anamukwiyila kwambili Solomo (1 Maf. 11:9, 10; w18.07 19 ¶9)

Zithunzi: Mlongo amene ni mbeta akucita phunzilo la munthu mwini, kwinaku akuganizila za m’bale winawake wosakwatila. 1. M’bale akupeleka ndemanga pa msonkhano wa mpingo. 2. Akucita ulaliki wapoyela. 3. Akugwila nawo nchito yokonza zinthu pa Nyumba ya Ufumu.

Mawu a Mulungu amalangiza Akhristu amene afuna kuloŵa m’banja kuti ayenela kukwatila “kokha mwa Ambuye.” (1 Akor. 7:39) Koma sikuti ngati munthu ni wobatizika, ndiye kuti basi angakhale mwamuna kapena mkazi woyenelela. Dzifunseni kuti, ‘Kodi munthuyu adzanithandiza kupitiliza kulambila Yehova na mtima wonse? Kodi waonetsa kwa utali wotani kuti amam’konda kwambili Yehova?’ Musanagwilizane zokwatilana na munthu, muyenela kukhala na nthawi yokwanila yomudziŵa bwino.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani