LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 September tsa. 8
  • Asa Anacita Zinthu Molimba Mtima—Kodi Inunso Mumatelo?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Asa Anacita Zinthu Molimba Mtima—Kodi Inunso Mumatelo?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Citani Zinthu Mwanzelu Panthawi ya Mtendele
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • Tumikilani Yehova ndi Mtima Wathunthu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Mmene Yehova Amayandikila kwa Ife
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Ni Nthawi Iti Pamene Tiyenela Kudalila Yehova?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 September tsa. 8

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Asa Anacita Zinthu Molimba Mtima—Kodi Inunso Mumatelo?

Mokangalika, Asa anakhalila kumbuyo kulambila koona (1 Maf. 15:11, 12; w12 8/15 8 ¶4)

Asa anasonyeza kuti anali kuona kulambila Yehova kukhala kofunika kwambili kuposa mgwilizano wake na acibale (1 Maf. 15:13; w17.03 19 ¶7)

Asa analakwitsapo zinthu zina. Koma Yehova anamuonabe kuti anali wokhulupilika cifukwa ca makhalidwe ake abwino (1 Maf. 15:14, 23; it-1 184-185)

Mwana wamwamuna akucoka pakhomo atanyamula cola ca katundu. Tate akutonthoza mkazi wake na mwana wake wamkazi amene akulila.

DZIFUNSENI KUTI: ‘Kodi kulambila koona nimakukondadi? Kodi nimaleka kugwilizana na aliyense amene wasiya Yehova, ngakhale amene ni wacibale wanga?’—2 Yoh. 9, 10.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani