LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 November tsa. 6
  • “N’cifukwa Ciyani Akhristu Ayenela Kuyesetsa Kuwonjezela Utumiki Wawo?”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “N’cifukwa Ciyani Akhristu Ayenela Kuyesetsa Kuwonjezela Utumiki Wawo?”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Alongo Angakalamile Bwanji?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • “Mwamuna Wake Amadziŵika Pazipata”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Kulitsani Makhalidwe Aumulungu—Cikhulupililo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Kalamilani Nchito Yabwino
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 November tsa. 6

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

“N’cifukwa Ciyani Akhristu Ayenela Kuyesetsa Kuwonjezela Utumiki Wawo?”

Abale na alongo amayesetsa kupita patsogolo kuti akwanilitse zolinga zawo zauzimu, monga kucitako upainiya, utumiki wa pa Beteli, komanso kumanga nawo Nyumba za Ufumu. Kuwonjezela apo, abale amayesetsa kuti akhale oyang’anila. (1 Tim. 3:1) Koma kodi izi zitanthauza kuti Akhristu ayenela kufunitsitsa udindo kapena utumiki winawake n’colinga cakuti ena aziwalemekeza?

ONELELANI VIDIYO YAKUTI N’CIFUKWA CIYANI TIYENELA KUYESETSA KUWONJEZELA UTUMIKI WATHU? (1 TIM. 3:1), KENAKO YANKHANI MAFUNSO AWA:

Kodi malemba awa aonetsa kuti ni zifukwa zitatu ziti zimatisonkhezela kuwonjezela utumiki wathu?

  • Mat. 5:14-16

  • 1 Tim. 4:15

  • Aheb. 5:14–6:1

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani