LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 November tsa. 14
  • Pemphelo Linasonkhezela Yehova Kucitapo Kanthu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pemphelo Linasonkhezela Yehova Kucitapo Kanthu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Nyamulani Mwana Wanu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Mulungu Athandiza Mfumu Hezekiya
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Yehova Anapangitsa Zinthu Zosayembekezeleka Kucitika
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Kuleza Mtima kwa Yehova Kuli na Malile
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 November tsa. 14
Mfumu Hezekiya akudwala ndipo akucondelela Yehova pamene ali pa bedi.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Pemphelo Linasonkhezela Yehova Kucitapo Kanthu

Yehova anauza Hezekiya kuti sacila matenda ake (2 Maf. 20:1; ip-1 394 ¶23)

Mwacikhulupililo, Hezekiya anapempha Yehova kuti akumbukile kukhulupilika kwake (2 Maf. 20:2, 3; w17.03 21 ¶16)

Mapemphelo a Hezekiya anasonkhezela Yehova kucitapo kanthu (2 Maf. 20:4-6; g01 7/22 13 ¶4)

Mapemphelo athu angasonkhezele Yehova kucita zinthu zimene sakanacita tikanapanda kum’pempha. Kodi cocitika ici cakuphunzitsani ciyani pa nkhani yocondelela Yehova m’pemphelo?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani