LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb23 July tsa. 7
  • Kodi Mumaona Kuti Nchito Yamanja si Yokuyenelelani?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Mumaona Kuti Nchito Yamanja si Yokuyenelelani?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Mukumbukila?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • Nehemiya Anali Kufuna Kutumikila Ena, Osati Kutumikilidwa
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Tsatilani Yehova na Mtima Wonse
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Khalanibe Acimwemwe Ngakhale Pamene Mwakumana na Zolefula
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
mwb23 July tsa. 7
Amuna na akazi aciisraeli akugwila nchito yomanganso mpanda wa Yerusalemu molimbika.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kodi Mumaona Kuti Nchito Yamanja si Yokuyenelelani?

Mkulu wa ansembe na abale ake sanadzione kuti anali apamwamba kwambili moti n’kulephela kumanga nawo mpanda wa Yerusalemu (Neh. 3:1)

Amuna ena otchuka sanadzicepetse kuti agwile nawo nchito yomanganso mpanda (Neh. 3:5; w06 2/1 10 ¶1)

Akazi oopa Mulungu anagwila nawo na mtima wonse nchito yolemetsa imeneyo (Neh. 3:12; w19.10 23 ¶11)

Nchito zambili zimene zimacitika mumpingo ni zamanja komanso zooneka ngati zapansi, ndipo nthawi zina ena sangaone nchitozo.—w04 8/1 18 ¶16.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi kugwila nchito zooneka ngati zapansi cifukwa ca uthenga wabwino nimakuona bwanji?’—1 Akor. 9:23.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani