LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb23 July tsa. 8
  • Nehemiya Anali Kufuna Kutumikila Ena, Osati Kutumikilidwa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Nehemiya Anali Kufuna Kutumikila Ena, Osati Kutumikilidwa
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Nkhani Zofanana
  • Mpanda Wa Yerusalemu
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • “Nthawi Yomweyo N’napemphela”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Mpanda wa Yerusalemu Umangidwanso
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Nehemiya anali woyang’anila wa citsanzo cabwino kwambili
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
mwb23 July tsa. 8
Nehemiya pamodzi na Aisiraeli ena akumanganso mpanda wa Yerusalemu.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Nehemiya Anali Kufuna Kutumikila Ena, Osati Kutumikilidwa

Nehemiya sanaone udindo wake monga popezela phindu (Neh. 5:14, 15, 17, 18; w02 11/1 27 ¶3)

Nehemiya sanali kungoyang’anila nchito, koma anali kugwila nawo (Neh. 5:16; w16.09 6 ¶16)

Nehemiya anapempha Yehova kuti akam’kumbukile cifukwa ca cikondi cake codzimana (Neh. 5:19; w00 2/1 32)

Ngakhale kuti Nehemiya anali bwanamkubwa, sanayembekezele kuti anthu azimupatsa ulemu wapadela. Iye ni citsanzo cabwino kwa onse amene ali na maudindo komanso mautumiki ena mumpingo.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi nimaganizila kwambili zimene ningacitile ena kuposa zimene nifuna kuti ena anicitile?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani