LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb23 July tsa. 10
  • “Cimwemwe Cimene Yehova Amapeleka Ndico Malo Anu Acitetezo”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Cimwemwe Cimene Yehova Amapeleka Ndico Malo Anu Acitetezo”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Nkhani Zofanana
  • Chimwemwe Chimene Yehova Amapereka
    Imbirani Yehova
  • Khalani Wokhulupilika kwa Yehova Posankha Mabwenzi
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • “Cimwemwe Cimene Yehova Amapeleka”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mmene Mungakhalile na Moyo Wopambana
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
mwb23 July tsa. 10
Ezara wanyamula mpukutu ndipo akutamanda Yehova pamaso pa anthu.

Ezara akuŵelengela anthu Cilamulo na kutamanda Yehova

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

“Cimwemwe Cimene Yehova Amapeleka Ndico Malo Anu Acitetezo”

Anthu anasonkhana kuti amvetsele pamene Ezara anali kuŵelenga Cilamulo (Neh. 8:1, 2; w13 10/1 19-20 ¶2; onani cithunzi pa cikuto)

Iyi inali nthawi yolambila Yehova mosangalala, osati yolila cifukwa cokumbukila macimo akale (Neh. 8:9, 11, 12)

Cimwemwe cimene Yehova amapeleka ni malo acitetezo kwa atumiki ake (Neh. 8:10; w07 7/15 22 ¶9-10)

Banja lacinyamata likuceza na banja lacikulile.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Nili na zifukwa zotani zokhalila wacimwemwe ngakhale kuti nimakumana na mavuto?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani