LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w23 February tsa. 32
  • Mfundo Yothandiza Yokhudza Webusaiti Yathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mfundo Yothandiza Yokhudza Webusaiti Yathu
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Tumitu
  • Nkhani Zofanana
  • Kupeza Nkhani Zimene Zinaikidwapo pa Webusaiti
  • Seŵenzetsani Tsamba Loyamba la JW.ORG mu Ulaliki
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Mfundo Yothandiza Pa Kuŵelenga Kwanu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Pezani Nzelu Zothandiza pa Umoyo pa JW.ORG
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zimene Si Zophunzila mu Nsanja ya Mlonda
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
Onaninso Zina
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
w23 February tsa. 32

Mfundo Yothandiza Yokhudza Webusaiti Yathu

Kupeza Nkhani Zimene Zinaikidwapo pa Webusaiti

Abale na alongo athu ambili amagwilitsa nchito nkhani zimene zimaikidwa patsamba loyamba pa webusaiti ya jw.org mu ulaliki. Iwo amatumikilako ena nkhanizo mosavuta kupitila pa zipangizo. Ndipo nthawi zambili, nkhanizo zimafotokoza mmene zocitika padzikoli zimakwanilitsila ulosi wa m’Baibo. M’bale wina analemba kuti: “Nkhani zoikidwa patsamba loyamba pa webusaiti yathu n’zimene zatithandiza kwambili pocita ulaliki m’njila imene tikucita palipano.”

Komabe, nkhani zimenezi zimasintha-sintha. Kodi mungazipeze kuti nkhani zimene sizikuonekelanso patsamba loyamba pa webusaiti yathu?

  • Pitani pa jw.org patsamba loyamba polemba kuti “Laibulale.” Kenako, dinizani link yakuti “Mpambo wa Nkhani.” Kenako, dinizani polemba kuti “Nkhani Zinanso.” Pamenepo mudzapeza nkhani zosiyanasiyana zimene zinaikidwa pa tsamba loyamba pa webusaiti yathu m’mbuyomu.

  • Pitani pa jw.org patsamba loyamba polemba kuti Laibulale. Kenako, dinizani link yakuti Mpambo wa Nkhani. Kenako, dinizani polemba kuti Nkhani Zinanso. Pamenepo mudzapeza nkhani zosiyanasiyana zimene zinaikidwa pa tsamba loyamba pa webusaiti yathu mbuyomu.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani