LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mrt nkhani 107
  • Yesu Adzathetsa Nkhondo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yesu Adzathetsa Nkhondo
  • Nkhani Zina
  • Nkhani Zofanana
  • Yesu Adzathetsa Umphawi
    Nkhani Zina
  • Kodi Ndani Adzapulumutsa Anthu?—Kodi Baibo Ikutipo Ciyani?
    Nkhani Zina
  • N’cifukwa Ninji Zandale Zikugaŵanitsa Anthu Conco?—Kodi Baibo Ikutipo Ciyani?
    Nkhani Zina
  • Ndani Amene Mungadalile?—Kodi Baibulo Ikutipo Ciyani?
    Nkhani Zina
Onaninso Zina
Nkhani Zina
mrt nkhani 107
Anyamata aŵili acicepele akhala moyandikana akuyang’ana malo ali patsogolo pawo owonongeka cifukwa ca nkhondo.

AspctStyle/stock.adobe.com

Yesu Adzathetsa Nkhondo

Pamene Yesu anali padziko lapansi, anaonetsa cikondi cacikulu pa anthu moti anapeleka moyo wake monga nsembe cifukwa ca iwo. (Mateyu 20:28; Yohane 15:13) Posacedwa, iye adzaonetsanso cikondi cake pa anthu poseŵenzetsa mphamvu zake monga Mfumu ya Ufumu wa Mulungu kuti athetse “nkhondo mpaka kumalekezelo a dziko lapansi.”—Salimo 46:9.

Onani zimene Yesu adzacita malinga n’zimene Baibo imakamba:

  • “Adzapulumutsa wosauka amene akufuula popempha thandizo, komanso wonyozeka ndi aliyense amene alibe womuthandiza. Adzamvela cisoni munthu wonyozeka ndi wosauka, ndipo adzapulumutsa miyoyo ya anthu osauka. Adzawapulumutsa kuti asapondelezedwe komanso kucitilidwa zaciwawa.”—Salimo 72:12-14.

Kodi tingaonetse bwanji kuti timayamikila zimene Yesu anaticitila komanso zimene adzaticitila m’tsogolo? Njila imodzi ndi mwakuphunzila zambili zokhuza “uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu,” umene Yesu anali kulalikila. (Luka 4:43) Welengani nkhani yakuti “Kodi Ufumu wa Mulungu N’chiyani?”

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani