LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mrt nkhani 108
  • Yesu Adzathetsa Umphawi

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yesu Adzathetsa Umphawi
  • Nkhani Zina
  • Nkhani Zofanana
  • Yesu Adzathetsa Nkhondo
    Nkhani Zina
  • Yesu Adzacotsapo Anthu Osamvela Malamulo
    Nkhani Zina
  • Ndani Amene Mungadalile?—Kodi Baibulo Ikutipo Ciyani?
    Nkhani Zina
  • Kuyankha Mafunso a M’baibulo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onaninso Zina
Nkhani Zina
mrt nkhani 108
Manja otambasula a munthu amene akupempha.

panitan/stock.adobe.com

Yesu Adzathetsa Umphawi

Yesu ali pa dziko lapansi, anaonetsa cikondi cacikulu kwa anthu, maka-maka osauka komanso acisoni cacikulu. (Mateyu 9:36) Anafika popeleka moyo wake kuti athandize anthu ena. (Mateyu 20:28; Yohane 15:13) Posacedwa, adzaonetsanso kuti amakonda anthu poseŵenzetsa ulamulilo wake na mphamvu zake monga Mfumu ya Ufumu wa Mulungu pothetsa umphawi pa dziko lonse lapansi.

Posewenzetsa mawu andakatulo, Baibo imafotokoza zimene Yesu adzacita. Imati:

  • “Ateteze anthu onyozeka pakati pa anthu, Apulumutse ana a anthu osauka.”—Salimo 72:4.

Kodi tingaonetse bwanji kuti timayamikila zimene Yesu anaticitila komanso zimene adzaticitila m’tsogolo? Njila ndi mwakuphunzila zambili zokhuza “uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu” umene Yesu anali kulalikila. (Luka 4:43) Welengani nkhani yakuti “Kodi Ufumu wa Mulungu N’chiyani?”

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani