LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 52
  • Tidzipeleka Monga Akhristu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tidzipeleka Monga Akhristu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tidzipereke Monga Akhristu
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    Imbirani Yehova
  • N’cifukwa Ciyani Muyenela Kudzipatulila na Kubatizika?
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 52

NYIMBO 52

Tidzipeleka Monga Akhristu

Yopulinta

(Aheberi 10:7, 9)

  1. 1. Yehova Mulungu wathu

    Ni Mlengi wa zonse,

    Zakumwamba na pa dziko—

    Zinthu zonse n’zake.

    Anatipatsanso moyo

    Kuti ‘se tidziŵe

    Iye ni Mulungu woona,

    Tidzamutumikila.

  2. 2. Yesu anabatizika.

    Anadzipeleka

    Kutumikila Yehova,

    Mpaka imfa yake.

    Analonjeza Yehova,

    Monga wodzozedwa,

    Kuti adzamutumikila

    Na moyo wake wonse.

  3. 3. Yehova, Atate wathu,

    Ise tadzikana.

    Tadzipeleka kwa imwe,

    Ndise anthu anu.

    Munatuma Mwana wanu,

    Kuti atifele.

    Na mitima yoyamikila,

    Tidzalambila imwe.

(Onaninso Mat. 16:24; Maliko 8:34; Luka 9:23.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani