LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 138
  • Kukongola kwa Imvi

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kukongola kwa Imvi
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Ulemerero Umene Umabwera Chifukwa cha Imvi
    Imbirani Yehova
  • Mvelani Pemphelo Langa Conde
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mulungu Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova
  • Ndimwe Mphamvu Zathu, Ciyembekezo, na Cidalilo Cathu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 138

NYIMBO 138

Kukongola kwa Imvi

Yopulinta

(Miyambo 16:31)

  1. 1. Pakati pathu pali

    Acikulile.

    Ngakhale avutike,

    Iwo safo’ka.

    Ena anafeledwa.

    Ena adwala.

    Yehova tipemphela,

    Atonthozeni.

    (KOLASI)

    Atate Yehova,

    Adalitseni.

    Auzeni kuti:

    “Mwagwila nchito.”

  2. 2. A imvi olungama

    Ni okongola.

    Yehova aŵakonda

    Sadzaŵasiya.

    Tiziŵayamikila

    Pa nchito zawo.

    Anadzipelekadi

    Na mphamvu zonse.

    (KOLASI)

    Atate Yehova,

    Adalitseni.

    Auzeni kuti:

    “Mwagwila nchito.”

(Onaninso Sal. 71:9, 18; Miy. 20:29; Mat. 25:21, 23; Luka 22:28; 1 Tim. 5:1.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani