LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 106
  • Kukulitsa Mkhalidwe wa Cikondi

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kukulitsa Mkhalidwe wa Cikondi
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tizisonyeza Chikondi
    Imbirani Yehova
  • “Mulungu Ndiye Chikondi”
    Imbirani Yehova
  • “Mulungu Ndiye Cikondi”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Cikondi Khalidwe Lamtengo Wapatali
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 106

NYIMBO 106

Kukulitsa Mkhalidwe wa Cikondi

Yopulinta

(1 Akorinto 13:1-8)

  1. 1. Tithandizeni kuonetsa

    Makhalidwe anu abwino.

    Koposa zonse tionetse

    Cikondi kwa abale athu.

    Ngati cikondi cazilala,

    Inu Yehova simukondwa.

    Tionjezeleni cikondi,

    Nthawi zonse ticionetse.

  2. 2. Cikondi cimatipangitsa

    Kuti tiganizile ena.

    Tikhululukila anzathu,

    Monga Yesu anakambila.

    Cikondi cimatithandiza

    Kupilila pamayeselo.

    Cikondi cipilila zonse

    Cikondi sicidzalephela.

(Onaninso Yoh. 21:17; 1 Akor. 13:13; Agal. 6:2.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani