LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 115
  • Tiyamikila Kuleza Mtima kwa Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tiyamikila Kuleza Mtima kwa Mulungu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tikuthokoza Mulungu Chifukwa cha Kuleza Mtima Kwake
    Imbirani Yehova
  • Cikumbutso Cimene Cikubwela Cidzatipatsa Mwai Woyamikila
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • “Yehova Ndidzamubwezela Ciani?”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • “Silidzacedwa!”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 115

NYIMBO 115

Tiyamikila Kuleza Mtima kwa Mulungu

Yopulinta

(2 Petulo 3:15)

  1. 1. O Yehova, wamphamvuzonse,

    Mumakonda cilungamo.

    Zoipa pano padziko

    M’lungu wathu zaculuka.

    Koma tidziŵa simucedwa;

    Mudzazicotsapo zoipa.

    (KOLASI)

    Yehova tiyamikila,

    Kuti ndinu woleza mtima.

  2. 2. Zaka cikwi kwa inu M’lungu

    Ni tsiku limodzi cabe.

    Tsiku lanu lalikulu;

    Posacedwa lidzafika.

    Inu simukonda zoipa,

    Koma mufuna ‘nthu alape.

    (KOLASI)

    Yehova tiyamikila,

    Kuti ndinu woleza mtima.

(Onaninso Neh. 9:30; Luka 15:7; 2 Pet. 3:8, 9.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani