LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 100
  • Alandileni na Manja Aŵili

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Alandileni na Manja Aŵili
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Alandireni Bwino
    Imbirani Yehova
  • Kucelezana ni Khalidwe Lofunika Kwambili
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Gaŵanani ndi Ena “Zabwino” mwa Kukhala Woceleza (Mat. 12:35a)
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tilalikile kwa Anthu a Makhalidwe Onse
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 100

NYIMBO 100

Alandileni na Manja Aŵili

Yopulinta

(Machitidwe 17:7)

  1. 1. Yehova amatilandila bwino.

    Amasamalila mosakondela.

    Mvula imagwabe,

    dzuŵa imawala;

    Amatipatsanso cakudya.

    Pamene tithandiza ovutika,

    Timatengela citsanzo ca M’lungu.

    Ngati tionetsa

    cifundo kwa ena,

    Yehova adzatidalitsa.

  2. 2. Pothandiza ena sitingadziŵe

    Zabwino zimene tingalandile.

    Ngakhale amene

    sitimaŵadziŵa

    Tifunika kuŵathandiza.

    Monga Lidiya tiziŵalandila,

    Akabwela tiziŵatsitsimula.

    Atate Yehova

    amaona onse

    Ocitila ena cifundo.

(Onaninso Mac. 16:14, 15; Aroma 12:13; 1 Tim. 3:2; Aheb. 13:2; 1 Pet. 4:9.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani