LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 108
  • Tamandani Yehova Chifukwa cha Ufumu Wake

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tamandani Yehova Chifukwa cha Ufumu Wake
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tamandani Ya Kaamba ka Mwana Wake Wodzozedwayo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tiyeni Tonse Titamande Ya
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tipita Nanu Limodzi
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 108

Nyimbo 108

Tamandani Yehova Chifukwa cha Ufumu Wake

(Chivumbulutso 21:2)

1. Yehova ’nadzoza Yesu

Kuti alamulire,

Kuti chifuniro cha M’lungu

Padzikoli chichitike.

(KOLASI)

Tamandani Yehova ndithu

Chifukwa cha Wodzozedwa

Inu nkhosa zokhulupirika

Zomvera malamulo.

Tamandani Wodzozedwayo,

Wolamula wakumwamba,

Amene adzayeretsa dzina

Loyera la Mulungu.

2. Abale a Yesu Khristu

Iwo ndi osankhika.

Adzalamulira ndi Yesu.

Dzikoli adzayeretsa.

(KOLASI)

Tamandani Yehova ndithu

Chifukwa cha Wodzozedwa

Inu nkhosa zokhulupirika

Zomvera malamulo.

Tamandani Wodzozedwayo,

Wolamula wakumwamba,

Amene adzayeretsa dzina

Loyera la Mulungu.

(Onaninso Miy. 29:4; Yes. 66:7, 8; Yoh. 10:4; Chiv. 5:9, 10.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani