LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 6
  • Pemphero la Mtumiki wa Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pemphero la Mtumiki wa Mulungu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Timatumikila Mulungu “Wacifundo Coculuka”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • “Uzikonda Yehova Mulungu Wako”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Mmene Tingalimbikitsile Cikondi Cathu pa Ena
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Anthu Achifundo Amakhala Odala
    Imbirani Yehova
Imbirani Yehova
sn nyimbo 6

Nyimbo 6

Pemphero la Mtumiki wa Mulungu

(Aefeso 6:18)

1. Atate wa kumwamba, Mfumu,

Dzina lanu litamandidwetu

Chifundo chanu ndi chosatha,

Komanso ndi chodalirika.

Inde n’chodalirika,

Chifundochi n’chosatha.

2. Mtima wathu uthandizeni

Kuti uzikonda choonadi.

Malamulo anu tisunge,

Nkhosa zanuzo tizifune.

Nkhosa zanu tifune,

Malamulo tisunge.

3. M’tipatse nzeru yakumwamba,

M’tidzaze ndi chikondi mumtima

M’tithandize kukonda anthu,

Onse adziwe M’lungu wathu.

Inde akudziweni,

Tiwakondedi anthu.

(Onaninso Sal. 143:10; Yoh. 21:15-17; Yak. 1:5.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani