LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 47
  • Pemphela kwa Yehova Tsiku na Tsiku

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pemphela kwa Yehova Tsiku na Tsiku
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Muzipemphera kwa Yehova Tsiku Lililonse
    Imbirani Yehova
  • Mwayi Wa Pemphelo
    Zimene Baibulo Ingatiphunzitse
  • Kodi Yehova Amamvetsela kwa Ife?
    Mvetselani kwa Mulungu Kuti Mukhale ndi Moyo Wamuyaya
  • Muyandikileni Mulungu Kupitila m’Pemphelo
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 47

NYIMBO 47

Pemphela kwa Yehova Tsiku na Tsiku

Yopulinta

(1 Atesalonika 5:17)

  1. 1. Pemphelani kwa Yehova M’lungu.

    Iye amamvela mapemphelo.

    Muuzeni za mumtima mwanu.

    Monga bwenzi lathu amamvela.

    Pemphelani kwa M’lungu.

  2. 2. Tipemphele kwa Yehova M’lungu,

    Tiyamikile mphatso ya moyo.

    Timupemphe cikhululukilo.

    Adziŵa kuti ndise ofo’ka.

    Pemphelani kwa M’lungu.

  3. 3. Pemphelani kwa Yehova M’lungu,

    Pamene imwe muli na vuto.

    Ni Atate wathu wacifundo.

    Iye adzakusamalilani.

    Pemphelani kwa M’lungu.

(Onaninso Sal. 65:5; Mat. 6:9-13; 26:41; Luka 18:1)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani