LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 39
  • Tipange Dzina Labwino na Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tipange Dzina Labwino na Mulungu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tipange Dzina Labwino kwa Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Kodi Dzina la Mulungu N’ndani?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2019
  • Yehova Akweza Dzina Lake
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulila
  • Kugwilitsila Nchito Dzina la Mulungu ndi Kudziŵa Tanthauzo Lake
    Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni-ceni
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 39

NYIMBO 39

Tipange Dzina Labwino na Mulungu

Yopulinta

(Mlaliki 7:1)

  1. 1. Timayesetsa tsiku lililonse,

    Kupanga dzina labwino na M’lungu.

    Tikapitiliza kumvela Yehova,

    Tikondweletsa mtima wake.

  2. 2. Kukondetsetsa zinthu za m’dzikoli,

    Kufunitsitsa kuti tilemele,

    Kulibe ubwino, tingasiye M’lungu.

    Sangatipatse madalitso.

  3. 3. Tifuna M’lungu atilembe dzina,

    Kuti tikhale mu buku la moyo.

    Lomba ndiye nthawi yakuti tipange

    Dzina labwino na Yehova.

(Onaninso Gen. 11:4; Miy. 22:1; Mal. 3:16; Chiv. 20:15.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani