LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 67
  • “Lalikila Mau”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Lalikila Mau”
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Lalikira Mawu”
    Imbirani Yehova
  • Kusakila Anthu Okonda Mtendele
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kusakila Anthu Okonda Mtendele
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Kodi Uthenga Wabwino Umalalikidwa Motani?
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 67

NYIMBO 67

“Lalikila Mau”

Yopulinta

(2 Timoteyo 4:2)

  1. 1. Mulungu watilamula

    Kuti tilalikile uthenga.

    Tilengeze kwa anthu onse,

    Adziŵe ciyembekezo cathu.

    (KOLASI)

    Lalikila,

    Kuti onse amvele!

    Lalika,

    Mapeto ayandika.

    Lalika,

    Ofatsa adzamvela.

    Lalika,

    Konse konse!

  2. 2. Anthu ena angaseke,

    Olo angafune kutitsutsa.

    Yehova adzatithandiza,

    Kuti tilalikile kwa onse.

    (KOLASI)

    Lalikila,

    Kuti onse amvele!

    Lalika,

    Mapeto ayandika.

    Lalika,

    Ofatsa adzamvela.

    Lalika,

    Konse konse!

  3. 3. Nthawi zina tidzapeza

    Ofuna kumvetsela uthenga.

    Iwo adzapulumukadi

    Tikaŵaphunzitsa coonadi.

    (KOLASI)

    Lalikila,

    Kuti onse amvele!

    Lalika,

    Mapeto ayandika.

    Lalika,

    Ofatsa adzamvela.

    Lalika,

    Konse konse!

(Onaninso Mat. 10:7; 24:14; Mac. 10:42; 1 Pet. 3:15.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani