LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 57
  • Tilalikile kwa Anthu a Makhalidwe Onse

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tilalikile kwa Anthu a Makhalidwe Onse
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tilalikile kwa Anthu a Makhalidwe Onse
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Yang’ana pa Mphoto
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Aphunzitseni Kucilimika
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 57

NYIMBO 57

Tilalikile kwa Anthu a Makhalidwe Onse

Yopulinta

(1 Timoteyo 2:4)

  1. 1. Tikhale anthu osakondela.

    Tikhale monga Mulungu wathu.

    Afuna onse apulumuke

    Na kukhala atumiki ake.

    (KOLASI)

    Si malo koma munthu;

    Si nkhope koma mtima.

    Tiuze anthu onse co’nadi.

    Timasakila anthu,

    Amene amafuna:

    “Kukhala mabwenzi a Yehova.”

  2. 2. Si kanthu mmene aonekela.

    Si kanthu kumene acokela.

    Mtima wawo ndiwo wofunika—

    Ni umene Yehova aona.

    (KOLASI)

    Si malo koma munthu;

    Si nkhope koma mtima.

    Tiuze anthu onse co’nadi.

    Timasakila anthu,

    Amene amafuna:

    “Kukhala mabwenzi a Yehova.”

  3. 3. Yehova amalandila onse

    Ofuna kukhala anthu ake.

    Tilalikile kwa anthu onse,

    Tiŵauze uthenga wabwino.

    (KOLASI)

    Si malo koma munthu;

    Si nkhope koma mtima.

    Tiuze anthu onse co’nadi.

    Timasakila anthu,

    Amene amafuna:

    “Kukhala mabwenzi a Yehova.”

(Onaninso Yoh. 12:32; Mac. 10:34; 1 Tim. 4:10; Tito 2:11.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani