LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 October tsa. 6
  • Muziyesetsa Kukhala Mwamtendele na Ena

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Muziyesetsa Kukhala Mwamtendele na Ena
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • “Ndakupatsani Citsanzo”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Tizithetsa Mikangano Mwamtendele
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
  • Mtendele Kodi Mungaupeze Bwanji?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 October tsa. 6

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MIYAMBO 17-21

Muziyesetsa Kukhala Mwamtendele na Ena

Mlongo apemphela, pambuyo pake akambilana na mlongo mnzake kuti athetse mkangano na kukhazikitsa mtendele

Anthu a Yehova amacita khama kuti akhale pa mtendele na anzawo. Nthawi zina, iwo amakangana ndi kukhumudwitsana kwambili. Koma malangizo ocokela m’Mau a Mulungu amawathandiza.

Akasiyana maganizo, Akhiristu okhulupilika amasunga mtendele mwa . . .

19:11

  • kukhala odekha

18:13, 17

  • kuonetsetsa kuti amvetsetsa nkhani yonse

17:9

  • kukhululukila amene awalakwila

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani