LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 May tsa. 6
  • Leka ‘Kufuna-funa Zinthu Zazikulu’

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Leka ‘Kufuna-funa Zinthu Zazikulu’
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Limbitsani Ubwenzi Pakati Panu Mapeto Asanafike
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • “Ine Ndili ndi Iwe Kuti Ndikulanditse”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 May tsa. 6

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YEREMIYA 44-48

Leka ‘Kufuna-funa Zinthu Zazikulu’

45:2-5

Baruki ayenela kuti anali nduna yophunzila bwino ya m’nyumba ya mfumu. Olo kuti anali kulambila Yehova ndi kuthandiza Yeremiya mokhulupilika, panthawi ina yake anacenjenekwa ndi zinthu zina. Iye anayamba kufuna-funa zinthu zazikulu,’ mwina kufuna udindo wokwelelapo m’bwalo la mfumu, kapena cuma. Anafunikila kusintha kalingalilidwe kake kuti apulumuke ciwonongeko ca Yerusalemu cimene cinali kubwela.

Pamene Baruki anali kalembela wa Yeremiya anayamba kufuna-funa zinthu zazikulu ndi kuchuka
Chati coonetsa nthawi imene Yeremiya anakhala mneneli, ndi pamene Baruki anakhala wothandiza wake, komanso pamene Yerusalemu anagwa
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani